Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 26:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Katani imeneyi uipachike pazipilala 4 za mtengo wa mthethe zokutidwa ndi golide. Tizitsulo tokolowekapo kataniyi tikhale tagolide. Zipilala zimenezi zikhale pazitsulo 4 zasiliva.

  • Ekisodo 26:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Nsalu yotchinga* khomo la chihema uipangire zipilala 5 za mtengo wa mthethe zokutidwa ndi golide. Tizitsulo tokolowekapo nsaluyo tikhale tagolide. Ndipo upange zitsulo 5 zakopa zokhazikapo zipilalazo.”

  • Ekisodo 36:37, 38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Atatero anawomba nsalu yotchinga khomo la chihema. Nsaluyo inali ya ulusi wabuluu, ya ubweya wa nkhosa wapepo, ulusi wofiira kwambiri ndi ulusi wopota wabwino kwambiri.+ 38 Anapanganso zipilala zake 5 ndi tizitsulo take tokolowekapo nsalu yotchingayo. Pamwamba pa zipilalazo anakutapo ndi golide komanso tizitsulo take tolumikizira anatikuta ndi golide. Koma zitsulo zake 5 zokhazikapo zipilalazo zinali zakopa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena