Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 25:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mukapange chihema chopatulika ndi ziwiya zake zonse mogwirizana ndendende ndi zimene ndikukusonyeza.+

  • Ekisodo 25:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Uonetsetse kuti wazipanga motsatira chitsanzo chimene wasonyezedwa mʼphiri.”+

  • 1 Mbiri 28:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anamupatsanso mapulani a kamangidwe ka zonse zimene anauzidwa kudzera mwa mzimu zokhudza mabwalo+ a nyumba ya Yehova, zipinda zonse zodyera kuzungulira kachisi, mosungira chuma cha nyumba ya Mulungu woona ndi mosungira zinthu zimene anaziyeretsa kuti zikhale zopatulika.+

  • 1 Mbiri 28:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Davide anati: “Dzanja la Yehova linali pa ine ndipo anandithandiza kuti ndidziwe zonse zokhudza mapulani a kamangidwe kake+ nʼkuwalemba.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena