Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mutenge amuna ena kuti akuthandizeni. Mutenge mwamuna mmodzi pafuko lililonse ndipo akhale mtsogoleri wa nyumba ya makolo ake.+

  • Numeri 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pa ana a Yosefe: kuchokera ku fuko la Efuraimu,+ Elisama mwana wa Amihudi, kuchokera ku fuko la Manase, Gamaliyeli mwana wa Pedazuri,

  • Numeri 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Amene azimanga msasa wawo kumadzulo ndi gulu la mafuko atatu la Efuraimu ndi magulu awo.* Mtsogoleri wa ana a Efuraimu ndi Elisama,+ mwana wa Amihudi.

  • Numeri 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Asilikali onse a gulu la Efuraimu amene anawalemba mayina alipo 108,100. Amenewa azikhala achitatu kunyamuka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena