Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno wansembe wa ku Midiyani+ anali ndi ana aakazi 7. Iwo anafika pachitsimepo kuti atunge madzi ndi kuwathira momwera ziweto kuti ziweto za bambo awo zimwe.

  • Ekisodo 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno atsikanawo atafika kunyumba, bambo awo a Reueli*+ anadabwa ndipo anati: “Bwanji mwabwerako mwamsanga chonchi lero?”

  • Ekisodo 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mose anakhala mʼbusa wa ziweto za Yetero*+ apongozi ake, wansembe wa ku Midiyani. Pamene ankaweta ziwetozo chakumadzulo kwa chipululu, anafika kuphiri la Mulungu woona, ku Horebe.+

  • Ekisodo 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno Yetero, wansembe wa ku Midiyani, apongozi ake a Mose,+ anamva zonse zimene Mulungu anachitira Mose ndi anthu ake Aisiraeli komanso mmene Yehova anawatulutsira ku Iguputo.+

  • Ekisodo 18:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho Yetero, apongozi ake a Mose, limodzi ndi ana aamuna a Mose ndi mkazi wake, anapita kwa Mose mʼchipululu, kuphiri la Mulungu woona, kumene anamanga msasa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena