Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 22:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Zimene muzichita ndi mwana woyamba kubadwa wa ngʼombe ndi wa nkhosa yanu ndi izi:+ Azikhala ndi mayi ake masiku 7. Pa tsiku la 8 muzimupereka kwa ine.+

  • Deuteronomo 15:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mwana aliyense wamphongo woyamba kubadwa wa ngʼombe kapena wa nkhosa muzimupatula nʼkumupereka kwa Yehova Mulungu wanu.+ Musamagwiritse ntchito iliyonse mwana woyamba kubadwa wa ngʼombe,* kapena kumeta ubweya wa mwana woyamba kubadwa wa nkhosa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena