-
Yoswa 13:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Kenako Mose anagawira cholowa fuko la Rubeni motsatira mabanja awo.
-
-
Yoswa 13:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 mizinda yonse ya mʼmalo okwera ndiponso dziko lonse la Sihoni mfumu ya Aamori imene inali kulamulira ili ku Hesiboni.+ Mfumu imeneyi Mose anaigonjetsa+ limodzi ndi atsogoleri a ku Midiyani, Evi, Rekemu, Zuri, Hura, ndi Reba.+ Amenewa anali mafumu omwe anali pansi pa ulamuliro wa Sihoni ndipo ankakhala mʼdzikolo.
-