Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Aroni anatenga Eliseba, mwana wamkazi wa Aminadabu, mchemwali wake wa Naasoni,+ kukhala mkazi wake. Ndipo Eliseba anamʼberekera Nadabu, Abihu, Eleazara ndi Itamara.+

  • Ekisodo 38:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mose analamula kuti awerengere zinthu zonse zimene anagwiritsa ntchito popanga chihema, kapena kuti chihema cha Umboni.+ Alevi ndi amene anachita zimenezi+ motsogoleredwa ndi Itamara+ mwana wa Aroni wansembe.

  • 1 Mbiri 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ana a Amuramu+ anali Aroni,+ Mose+ ndi Miriamu.+ Ana a Aroni anali Nadabu, Abihu,+ Eliezara+ ndi Itamara.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena