Ekisodo 13:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Pofuna kuwatsogolera, Yehova ankayenda patsogolo pawo. Masana ankawatsogolera pogwiritsa ntchito chipilala cha mtambo+ ndipo usiku ankawatsogolera pogwiritsa ntchito chipilala cha moto kuti chiziwaunikira. Choncho ankatha kuyenda masana komanso usiku.+ Ekisodo 23:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Ndikukutumizirani mngelo patsogolo panu+ kuti azikutetezani mʼnjira komanso kukakulowetsani mʼdziko limene ndakukonzerani.+ Ekisodo 29:45 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 45 Ndidzakhala pakati pa Aisiraeli ndipo ndidzakhala Mulungu wawo.+ Yesaya 8:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Konzani pulani, koma idzalephereka. Nenani zimene mukufuna, koma sizidzachitika,Chifukwa Mulungu ali nafe.*+
21 Pofuna kuwatsogolera, Yehova ankayenda patsogolo pawo. Masana ankawatsogolera pogwiritsa ntchito chipilala cha mtambo+ ndipo usiku ankawatsogolera pogwiritsa ntchito chipilala cha moto kuti chiziwaunikira. Choncho ankatha kuyenda masana komanso usiku.+
20 Ndikukutumizirani mngelo patsogolo panu+ kuti azikutetezani mʼnjira komanso kukakulowetsani mʼdziko limene ndakukonzerani.+
10 Konzani pulani, koma idzalephereka. Nenani zimene mukufuna, koma sizidzachitika,Chifukwa Mulungu ali nafe.*+