Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 35:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ana aamuna amene Leya anaberekera Yakobo anali Rubeni+ mwana wake woyamba, kenako Simiyoni, Levi, Yuda, Isakara ndi Zebuloni.

  • Genesis 46:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ana a Simiyoni+ anali Yemueli, Yamini, Ohadi, Yakini, Zohari ndi Shauli+ mwana wa mkazi wa Chikanani.

  • Ekisodo 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ana aamuna a Simiyoni anali Yemueli, Yamini, Ohadi, Yakini, Zohari ndi Shauli, mwana amene anabereka ndi mkazi wa Chikanani.+ Amenewa ndi mabanja a fuko la Simiyoni.

  • 1 Mbiri 4:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ana a Simiyoni+ anali Nemueli, Yamini, Yaribi, Zera ndi Shauli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena