Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 38:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Koma mwanayo anabweza dzanja lake. Nthawi yomweyo mchimwene wake anatuluka, moti mzambayo anafuula kuti: “Bwanji ukuchita kungʼamba njira?” Nʼchifukwa chake anamupatsa dzina lakuti Perezi.*+

  • Rute 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mzere wa ana a Perezi+ unayenda chonchi: Perezi anabereka Hezironi,+

  • Mateyu 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yuda anabereka Perezi ndi Zera,+ ndipo mayi awo anali Tamara.

      Perezi anabereka Hezironi.+

      Hezironi anabereka Ramu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena