Hoseya 2:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Mayiyu ndidzamudzala ngati mbewu zanga padziko lapansi.+Ndidzachitira chifundo amene sanasonyezedwe chifundo.*Ndipo ndidzauza anthu amene si anthu anga kuti: “Ndinu anthu anga,”*+ Iwo adzayankha kuti: “Inu ndinu Mulungu wathu.”’”+ Aroma 9:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Ndi zofanananso ndi zimene ananena mʼbuku la Hoseya kuti: “Anthu amene si anthu anga+ ndidzawatchula kuti ‘anthu anga,’ ndipo mkazi amene sankakondedwa ndidzamutchula kuti ‘wokondedwa.’+ Aroma 11:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndiyeno ndifunse kuti, kodi anapunthwa mpaka kugweratu? Ayi. Koma chifukwa cha kulakwa kwawo anthu a mitundu ina apeza chipulumutso, ndipo zimenezi zachititsa kuti olakwawo achite nsanje.+ 1 Petulo 2:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Poyamba simunali anthu a Mulungu, koma tsopano ndinu anthu ake.+ Mulungu anali asanakuchitireni chifundo, koma tsopano wakuchitirani chifundo.+
23 Mayiyu ndidzamudzala ngati mbewu zanga padziko lapansi.+Ndidzachitira chifundo amene sanasonyezedwe chifundo.*Ndipo ndidzauza anthu amene si anthu anga kuti: “Ndinu anthu anga,”*+ Iwo adzayankha kuti: “Inu ndinu Mulungu wathu.”’”+
25 Ndi zofanananso ndi zimene ananena mʼbuku la Hoseya kuti: “Anthu amene si anthu anga+ ndidzawatchula kuti ‘anthu anga,’ ndipo mkazi amene sankakondedwa ndidzamutchula kuti ‘wokondedwa.’+
11 Ndiyeno ndifunse kuti, kodi anapunthwa mpaka kugweratu? Ayi. Koma chifukwa cha kulakwa kwawo anthu a mitundu ina apeza chipulumutso, ndipo zimenezi zachititsa kuti olakwawo achite nsanje.+
10 Poyamba simunali anthu a Mulungu, koma tsopano ndinu anthu ake.+ Mulungu anali asanakuchitireni chifundo, koma tsopano wakuchitirani chifundo.+