Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Yehova adzakumenyerani nkhondo,+ ndipo inu mudzangokhala phee, osachita chilichonse.”

  • Ekisodo 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yehova ndi msilikali wamphamvu.+ Dzina lake ndi Yehova.+

  • Deuteronomo 1:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Yehova Mulungu wanu adzakutsogolerani ndipo adzakumenyerani nkhondo,+ ngati mmene anachitira ku Iguputo inu mukuona.+

  • Deuteronomo 20:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 chifukwa Yehova Mulungu wanu akuyenda nanu limodzi kuti akumenyereni nkhondo nʼkukupulumutsani kwa adani anu.’+

  • Yoswa 10:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Yoswa anagonjetsa mafumu onsewa nʼkulanda malo awo pa nthawi imodzi, chifukwa Yehova Mulungu wa Isiraeli ndi amene ankawamenyera nkhondo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena