Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 46:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ana amene Yosefe anabereka ku Iguputo analipo awiri. Anthu onse amʼnyumba ya Yakobo amene anali nawo ku Iguputo analipo 70.+

  • Ekisodo 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ana onse a Yakobo komanso zidzukulu zake* analipo 70, koma Yosefe anali kale ku Iguputo.+

  • Machitidwe 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho Yosefe anatumiza anthu ku Kanani kukatenga bambo ake Yakobo ndiponso abale ake onse.+ Ndipo onse pamodzi analipo anthu 75.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena