Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 17:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 ndiye munthu wina akakuuzani zimenezi kapena mwamva zimene zachitika, muzifufuza nkhaniyo mosamala. Mukatsimikizira kuti ndi zoonadi+ kuti chinthu choipachi chachitika mu Isiraeli, 5 muzitenga mwamuna kapena mkazi amene wachita chinthu choipayo nʼkupita naye kunja kwa mzinda, ndipo muzikamuponya miyala kuti afe.+

  • 2 Mbiri 28:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Peka+ mwana wa Remaliya anapha anthu 120,000 ku Yuda tsiku limodzi ndipo onsewa anali amuna olimba mtima. Iwo anaphedwa chifukwa chakuti anasiya Yehova Mulungu wa makolo awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena