Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 22:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Musamaphe ngʼombe kapena nkhosa ndi mwana wake pa tsiku limodzi.+

  • Salimo 145:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova ndi wabwino kwa aliyense,+

      Ndipo ntchito zake zonse zimasonyeza kuti ndi wachifundo.

  • Miyambo 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Wolungama amasamalira ziweto zake,+

      Koma munthu woipa amaganiza kuti ndi wachifundo, pamene ali wankhanza.

  • Mateyu 10:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mpheta ziwiri amazigulitsa kakhobidi kamodzi kochepa mphamvu,* si choncho? Koma palibe ngakhale imodzi imene idzagwa pansi Atate wanu osadziwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena