Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 21:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Munthu akakhala ndi chilema chilichonse, asayandikire malo opatulika. Kaya akhale ndi vuto losaona, wolumala, wankhope yopotoka,* wamkono kapena mwendo wautali kwambiri kuposa unzake,

  • Levitiko 21:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 wa linunda, wamfupi kwambiri,* wa diso lolumala, wa zikanga, wa zipere ndi wa mavalo owonongeka.+

  • Yesaya 56:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Izi nʼzimene Yehova wanena kwa anthu ofulidwa amene amasunga sabata langa. Amene asankha kuchita zimene ndimasangalala nazo komanso amene amatsatira pangano langa:

       5 “Mʼnyumba mwanga ndiponso mkati mwa mpanda wanga ndidzawapatsa chipilala chachikumbutso ndiponso dzina,

      Zomwe ndi zabwino kwambiri kuposa ana aamuna ndi aakazi.

      Ndidzawapatsa dzina limene lidzakhalapo mpaka kalekale,

      Dzina limene silidzatha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena