Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 14:28, 29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Kumapeto kwa zaka zitatu zilizonse muzidzabweretsa chakhumi cha zokolola zanu zonse mʼchaka chachitatucho, ndipo muzidzachisiya mkati mwa mzinda wanu.+ 29 Ndiyeno Mlevi, amene sanapatsidwe gawo kapena cholowa ngati inuyo, komanso mlendo, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye amene akukhala mumzinda wanu, azibwera kudzadya ndi kukhuta+ kuti Yehova Mulungu wanu akudalitseni pa chilichonse chimene mukuchita.”+

  • Miyambo 14:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Munthu amene amanyoza mnzake ndiye kuti akuchimwa,

      Koma wosangalala ndi munthu amene amakomera mtima anthu onyozeka.+

  • 1 Yohane 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Aliyense amene ali ndi zinthu zofunika pa moyo ndipo akuona mʼbale wake akuvutika chifukwa chosowa zinthuzo, koma osamusonyeza chifundo, kodi tingati munthu ameneyu amakonda Mulungu?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena