-
Yeremiya 29:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 ‘Ndidzawathamangitsa ndi lupanga,+ njala ndi mliri ndipo ndidzawapangitsa kuti akhale chinthu chochititsa mantha kwa maufumu onse apadziko lapansi.+ Komanso ndidzawachititsa kuti akhale chinthu chotembereredwa, chodabwitsa, chochiimbira mluzu+ ndiponso kuchinyoza pakati pa mitundu yonse ya anthu kumene ndidzawabalalitsireko.+
-