Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 29:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 ‘Ndidzawathamangitsa ndi lupanga,+ njala ndi mliri ndipo ndidzawapangitsa kuti akhale chinthu chochititsa mantha kwa maufumu onse apadziko lapansi.+ Komanso ndidzawachititsa kuti akhale chinthu chotembereredwa, chodabwitsa, chochiimbira mluzu+ ndiponso kuchinyoza pakati pa mitundu yonse ya anthu kumene ndidzawabalalitsireko.+

  • Luka 21:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Anthu adzaphedwa ndi lupanga ndiponso kutengedwa ukapolo kupita nawo ku mitundu ina yonse.+ Anthu a mitundu ina adzapondaponda Yerusalemu mpaka nthawi zoikidwiratu za anthu a mitundu inawo zitakwanira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena