-
Numeri 22:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Ndiyeno buluyo ataona mngelo wa Yehova ataima pamsewu lupanga lake lili mʼmanja, anayesa kuchoka mumsewu nʼkupatukira kutchire. Koma Balamu anayamba kumʼkwapula kuti abwerere mumsewu.
-