Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 28:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Afilisiti anasonkhana nʼkukamanga msasa ku Sunemu.+ Nayenso Sauli anasonkhanitsa Aisiraeli onse nʼkukamanga msasa ku Giliboa.+

  • 1 Mafumu 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno anafufuza mtsikana wokongola mʼdziko lonse la Isiraeli. Kenako anapeza Abisagi+ wa ku Sunemu+ ndipo anabwera naye kwa mfumu.

  • 2 Mafumu 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsiku lina Elisa anapita ku Sunemu.+ Kumeneko kunali mayi wina wodziwika. Mayiyo anaumiriza Elisa kuti adye chakudya.+ Nthawi zonse Elisa akamadutsa, ankaima kunyumba kwa mayiyo kuti adye chakudya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena