Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 21:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho Aisiraeli anachita maere nʼkupatsa Alevi mizinda imeneyi ndi malo ake odyetserako ziweto, mogwirizana ndi zimene Yehova analamula kudzera mwa Mose.+

  • Yoswa 21:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kuchokera mʼfuko la Rubeni, anawapatsa Bezeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto, Yahazi ndi malo ake odyetserako ziweto,+

  • 1 Mbiri 6:77, 78
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 77 Kuchokera ku fuko la Zebuloni,+ anapatsa anthu a ku banja la Merari amene anatsala, mzinda wa Rimono ndi malo ake odyetserako ziweto ndiponso mzinda wa Tabori ndi malo ake odyetserako ziweto. 78 Kuchokera ku fuko la Rubeni, anawapatsa mzinda wa Bezeri mʼchipululu ndi malo ake odyetserako ziweto. Mzindawo unali mʼchigawo cha Yorodano pafupi ndi Yeriko chakumʼmawa kwa Yorodano. Anawapatsanso mzinda wa Yahazi+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena