Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 16:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mngelo wa Yehovayo ananenanso kuti: “Taona, panopa ndiwe woyembekezera, ndipo udzabereka mwana wamwamuna. Mwanayo udzamʼpatse dzina lakuti Isimaeli,* chifukwa Yehova wamva kulira kwako.

  • Genesis 25:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mayina a ana a Isimaeli, malinga ndi mabanja awo ndi awa: Nebayoti,+ mwana woyamba wa Isimaeli, Kedara,+ Adibeele, Mibisamu,+

  • Genesis 28:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Choncho Esau anapita kwa Isimaeli* nʼkukatengako mkazi wina kuwonjezera pa akazi amene anali nawo. Mkaziyo dzina lake anali Mahalati ndipo anali mchemwali wake wa Nebayoti. Mahalati anali mwana wa Isimaeli, mwana wa Abulahamu.+

  • Genesis 37:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pamene amalonda a Chimidiyani+ aja ankadutsa, abale a Yosefe anamutulutsa mʼchitsimemo nʼkumugulitsa kwa Aisimaeliwo. Anamugulitsa ndalama zasiliva 20,+ ndipo amalondawo anapita naye ku Iguputo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena