Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 6:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iwo anayankha kuti: “Ngati mukubweza likasa lapangano la Yehova Mulungu wa Isiraeli, musalibweze popanda kupereka nsembe. Mulimonse mmene zingakhalire, muyenera kupereka nsembe yakupalamula.+ Mukatero mudzachira ndipo mudzadziwa chifukwa chake dzanja lake silinasiye kukukhaulitsani.” 4 Ndiyeno iwo anafunsa kuti: “Kodi nsembe yakupalamula imene tiyenera kumutumizira ikhale chiyani?” Poyankha, ansembe ndi olosera aja anati: “Mutumize zifaniziro 5 zagolide za matenda a mudzi, ndi zifaniziro 5 zagolide za mbewa, mogwirizana ndi chiwerengero cha olamulira a Afilisiti.+ Muchite zimenezi chifukwa mliriwu wagwera aliyense wa inu, pamodzi ndi olamulira anu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena