Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Mawa cha nthawi ngati ino ndidzakutumizira munthu kuchokera kudera la Benjamini.+ Udzamudzoze kuti akhale mtsogoleri wa anthu anga Aisiraeli.+ Iye adzapulumutsa anthu anga mʼmanja mwa Afilisiti, chifukwa ndaona mmene akuvutikira ndiponso ndamva kulira kwawo.”+

  • Machitidwe 13:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma kenako anthuwo ananena kuti akufuna mfumu.+ Choncho Mulungu anawapatsa Sauli mwana wa Kisi, munthu wa fuko la Benjamini,+ ndipo anakhala mfumu yawo kwa zaka 40.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena