Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 36:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndikunena zoona, mawu anga si onama.

      Amene amadziwa chilichonse+ akukuonani.

  • Yobu 37:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kodi mukudziwa chimene chimachititsa kuti mitambo izikhala mʼmalere?+

      Zimenezi ndi ntchito zodabwitsa za Mulungu amene amadziwa chilichonse.+

  • Aroma 11:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndithudi, madalitso amene Mulungu amapereka ndi ochuluka kwambiri. Nzeru zake nʼzozama, ndiponso iye ndi wodziwa zinthu kwambiri. Ziweruzo zake ndi zovuta kuzimvetsa, ndipo ndani angatulukire njira zake?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena