Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Nʼchifukwa chake ndalumbirira nyumba ya Eli kuti machimo a anthu a mʼnyumba ya Eli sadzaphimbidwa ndi nsembe ina iliyonse.”+

  • 1 Samueli 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Komanso Likasa la Mulungu linalandidwa, ndipo Hofeni ndi Pinihasi, ana a Eli, anaphedwa.+

  • 1 Samueli 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Munthuyo atangotchula za Likasa la Mulungu woona, Eli, yemwe anali pageti anagwa chagada kuchoka pampando. Khosi lake linathyoka ndipo anafa chifukwa anali wokalamba ndiponso wonenepa kwambiri. Eli anaweruza Isiraeli kwa zaka 40.

  • 1 Samueli 22:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno mfumu inauza Doegi+ kuti: “Iwe, ipha ansembewa!” Nthawi yomweyo Doegi wa ku Edomu+ anapha ansembewo. Tsiku limenelo anapha amuna 85 ovala efodi wa nsalu.+

  • 1 Mafumu 2:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Choncho Solomo anachotsa Abiyatara kuti asatumikirenso monga wansembe wa Yehova ndipo izi zinakwaniritsa mawu amene Yehova analankhula ku Silo+ okhudza nyumba ya Eli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena