Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 18:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsiku lotsatira, Sauli anagwidwa ndi mzimu woipa wochokera kwa Mulungu+ moti anayamba kuchita zinthu zachilendo* mʼnyumba mwake. Pa nthawiyi nʼkuti Davide akuimba nyimbo ndi zeze+ ngati mmene ankachitira ndipo Sauli anali ndi mkondo mʼmanja mwake.+ 11 Kenako Sauli anaponya mkondowo+ ndipo mumtima mwake ankati: ‘Ndibaya Davide nʼkumukhomerera kukhoma!’ Koma Davide anazinda nʼkuthawa ndipo zimenezi zinachitika kawiri konse.

  • 1 Samueli 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiyeno Davide anathawa kuchoka ku Nayoti, ku Rama. Koma anapita kwa Yonatani nʼkumuuza kuti: “Kodi ine ndatani?+ Ndalakwa chiyani, ndipo bambo ako ndawalakwira chiyani kuti azifuna kundipha?”

  • 1 Samueli 20:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Atatero, Sauli anaponya mkondo wake kuti amuphe.+ Apa tsopano Yonatani anadziwa kuti bambo ake atsimikiza zopha Davide.+

  • 1 Samueli 23:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamene Davide anali mʼchipululu cha Zifi ku Horesi, anadziwa kuti* Sauli ali mʼderalo ndipo akufunafuna moyo wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena