Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsiku lachitatu, munthu wina anabwera kuchokera kumsasa wa Sauli. Iye anali atangʼamba zovala zake komanso atadzithira dothi kumutu. Atafika kwa Davide, anagwada nʼkuwerama mpaka nkhope yake kufika pansi, kenako anagona pansi.

  • 2 Samueli 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno Davide anamufunsa kuti: “Zayenda bwanji kumeneko? Chonde, ndiuze.” Iye anayankha kuti: “Anthu athawa kunkhondo komanso anthu ambiri aphedwa. Nayenso Sauli ndi mwana wake Yonatani afa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena