Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 1:13-15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno Davide anafunsa mnyamata amene anabweretsa uthengawo kuti: “Kodi kwanu nʼkuti?” Iye anayankha kuti: “Ndine mwana wa Mwamaleki, amene anabwera kudzakhala ndi Aisiraeli.” 14 Davide anamufunsa kuti: “Nʼchifukwa chiyani sunaope kupha wodzozedwa wa Yehova?”+ 15 Atatero, Davide anaitana mmodzi mwa anyamata ake nʼkumuuza kuti: “Bwera kuno udzamuphe.” Choncho iye anamuphadi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena