Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 17:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma iye asakhale ndi mahatchi ambiri+ kapena kuchititsa anthu kuti abwerere ku Iguputo kuti akatenge mahatchi ochuluka+ chifukwa Yehova anakuuzani kuti, ‘Musabwererenso kudzera njira iyi.’

  • Salimo 20:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ena amadalira magaleta ndipo ena amadalira mahatchi,+

      Koma ife timadalira dzina la Yehova Mulungu wathu.+

  • Salimo 33:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Si nzeru kudalira hatchi chifukwa singapulumutse munthu,+

      Mphamvu zake zochuluka sizingapulumutse munthu

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena