1 Samueli 26:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndiyeno Davide anauza Ahimeleki Muhiti+ ndi Abisai+ mwana wa Zeruya,+ mchimwene wake wa Yowabu, kuti: “Ndani apite nane kwa Sauli kumsasa?” Abisai anayankha kuti: “Ine ndipita nanu.” 2 Samueli 2:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Ana atatu aamuna a Zeruya,+ omwe ndi Yowabu,+ Abisai+ ndi Asaheli+ analinso pompo. Asaheli anali waliwiro kwambiri ngati mbawala. 2 Samueli 23:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Abisai,+ mchimwene wake wa Yowabu mwana wa Zeruya+ anali mtsogoleri wa anthu ena atatu. Iye anatenga mkondo wake nʼkupha anthu 300. Abisai anali wotchuka ngati amuna atatu aja.+ 1 Mbiri 2:15, 16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 wa 6 Ozemu ndipo wa 7 anali Davide.+ 16 Azichemwali awo anali Zeruya ndi Abigayeli.+ Zeruya anali ndi ana atatu: Abisai,+ Yowabu+ ndi Asaheli.+
6 Ndiyeno Davide anauza Ahimeleki Muhiti+ ndi Abisai+ mwana wa Zeruya,+ mchimwene wake wa Yowabu, kuti: “Ndani apite nane kwa Sauli kumsasa?” Abisai anayankha kuti: “Ine ndipita nanu.”
18 Ana atatu aamuna a Zeruya,+ omwe ndi Yowabu,+ Abisai+ ndi Asaheli+ analinso pompo. Asaheli anali waliwiro kwambiri ngati mbawala.
18 Abisai,+ mchimwene wake wa Yowabu mwana wa Zeruya+ anali mtsogoleri wa anthu ena atatu. Iye anatenga mkondo wake nʼkupha anthu 300. Abisai anali wotchuka ngati amuna atatu aja.+
15 wa 6 Ozemu ndipo wa 7 anali Davide.+ 16 Azichemwali awo anali Zeruya ndi Abigayeli.+ Zeruya anali ndi ana atatu: Abisai,+ Yowabu+ ndi Asaheli.+