Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 17:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako Husai anauza Zadoki ndi Abiyatara+ ansembe kuti: “Ahitofeli wapereka malangizo akutiakuti kwa Abisalomu ndi akulu a Isiraeli koma ine ndapereka malangizo akutiakuti.

  • 2 Samueli 19:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mfumu Davide inatumiza uthenga kwa Zadoki+ ndi Abiyatara+ ansembe wakuti: “Muwafunse akulu a Yuda+ kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani inu nokha simukuchita chilichonse kuti mfumu ibwerere kunyumba yake, pamene Aisiraeli onse atumiza uthenga kwa mfumu?

  • 1 Mafumu 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Benaya+ mwana wa Yehoyada anali mkulu wa asilikali, ndipo Zadoki ndi Abiyatara+ anali ansembe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena