Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 13:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mʼchaka cha 23 cha Yehoasi+ mwana wa Ahaziya+ mfumu ya Yuda, Yehoahazi mwana wa Yehu+ anakhala mfumu ya Isiraeli ku Samariya ndipo analamulira kwa zaka 17.

  • 2 Mafumu 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yehoasi+ mwana wa Yehoahazi anakhala mfumu ya Isiraeli ku Samariya mʼchaka cha 37 cha Yehoasi mfumu ya Yuda ndipo analamulira kwa zaka 16.

  • 2 Mafumu 14:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mʼchaka cha 15 cha Amaziya mwana wa Yehoasi mfumu ya Yuda, Yerobowamu+ mwana wa Yehoasi mfumu ya Isiraeli anakhala mfumu ku Samariya ndipo analamulira zaka 41.

  • 2 Mafumu 15:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mʼchaka cha 38 cha Azariya+ mfumu ya Yuda, Zekariya+ mwana wa Yerobowamu anakhala mfumu ya Isiraeli ku Samariya ndipo analamulira miyezi 6.

  • 2 Mafumu 15:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Izi zinakwaniritsa mawu amene Yehova anauza Yehu akuti: “Ana ako aamuna adzakhala pampando wachifumu wa Isiraeli+ mpaka mʼbadwo wa 4.”+ Ndipo zimenezi ndi zomwe zinachitikadi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena