Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 ndikupatsa zimene wapempha.+ Ndikupatsa mtima wanzeru ndi womvetsa zinthu+ kuposa anthu onse amene anakhalapo mʼmbuyomu komanso amene adzakhaleko mʼtsogolo.+

  • 2 Mbiri 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Ufumu wa Solomo mwana wa Davide unakhala wamphamvu. Yehova Mulungu wake anali naye ndipo anamuchititsa kukhala wamphamvu kwambiri.+

  • 2 Mbiri 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 ndikupatsa nzeru ndi luso lodziwa zinthu. Ndikupatsanso katundu, chuma ndi ulemu zochuluka kwambiri kuposa zimene anali nazo mafumu amene anakhalako iwe usanakhaleko ndiponso zoposa zimene aliyense wobwera pambuyo pako adzakhale nazo.”+

  • Mlaliki 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndinali ndi zinthu zambiri kuposa aliyense amene anakhalapo mu Yerusalemu+ ine ndisanakhalepo. Ndipo ndinapitiriza kuchitabe zinthu mwanzeru.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena