1 Samueli 24:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Yehova aweruze pakati pa ine ndi inu,+ ndipo Yehova abwezere mʼmalo mwa ine,+ koma dzanja langali silidzakuchitirani choipa.+ 1 Samueli 24:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Yehova akhale woweruza, ndipo aweruze pakati pa ine ndi inu. Iye adzaona nkhaniyi nʼkundiweruza kuti ndine wosalakwa+ ndipo adzandipulumutsa mʼmanja mwanu.” 1 Samueli 26:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Yehova ndi amene adzabwezera aliyense mogwirizana ndi chilungamo chake+ komanso kukhulupirika kwake. Lero Yehova anakuperekani mʼmanja mwanga, koma sindinafune kuvulaza wodzozedwa wa Yehova.+ Salimo 7:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Nyamukani mutakwiya, inu Yehova.Imirirani ndi kukhaulitsa adani anga amene andikwiyira.+Dzukani nʼkundithandiza, ndipo mulamule kuti chilungamo chichitike.+
12 Yehova aweruze pakati pa ine ndi inu,+ ndipo Yehova abwezere mʼmalo mwa ine,+ koma dzanja langali silidzakuchitirani choipa.+
15 Yehova akhale woweruza, ndipo aweruze pakati pa ine ndi inu. Iye adzaona nkhaniyi nʼkundiweruza kuti ndine wosalakwa+ ndipo adzandipulumutsa mʼmanja mwanu.”
23 Yehova ndi amene adzabwezera aliyense mogwirizana ndi chilungamo chake+ komanso kukhulupirika kwake. Lero Yehova anakuperekani mʼmanja mwanga, koma sindinafune kuvulaza wodzozedwa wa Yehova.+
6 Nyamukani mutakwiya, inu Yehova.Imirirani ndi kukhaulitsa adani anga amene andikwiyira.+Dzukani nʼkundithandiza, ndipo mulamule kuti chilungamo chichitike.+