Levitiko 26:7, 8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Mudzathamangitsa adani anu ndi kuwagonjetsa ndi lupanga. 8 Anthu anu 5 adzathamangitsa adani 100, ndipo anthu 100 adzathamangitsa adani 10,000, moti mudzagonjetsa adani anu ndi lupanga.+ Deuteronomo 28:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Yehova adzachititsa adani anu amene adzakuukireni kugonja pamaso panu.+ Pobwera kudzakuukirani adzadutsa njira imodzi, koma pothawa pamaso panu, adzadutsa njira zosiyanasiyana 7.+ 2 Samueli 10:13, 14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Kenako Yowabu ndi amuna amene anali naye anapita kukamenyana ndi Asiriya ndipo Asiriyawo anayamba kuthawa.+ 14 Aamoni ataona kuti Asiriya athawa, nawonso anathawa Abisai nʼkupita mumzinda. Yowabu atamaliza kumenyana ndi Aamoni anabwerera ku Yerusalemu.
7 Mudzathamangitsa adani anu ndi kuwagonjetsa ndi lupanga. 8 Anthu anu 5 adzathamangitsa adani 100, ndipo anthu 100 adzathamangitsa adani 10,000, moti mudzagonjetsa adani anu ndi lupanga.+
7 Yehova adzachititsa adani anu amene adzakuukireni kugonja pamaso panu.+ Pobwera kudzakuukirani adzadutsa njira imodzi, koma pothawa pamaso panu, adzadutsa njira zosiyanasiyana 7.+
13 Kenako Yowabu ndi amuna amene anali naye anapita kukamenyana ndi Asiriya ndipo Asiriyawo anayamba kuthawa.+ 14 Aamoni ataona kuti Asiriya athawa, nawonso anathawa Abisai nʼkupita mumzinda. Yowabu atamaliza kumenyana ndi Aamoni anabwerera ku Yerusalemu.