Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 8:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mfumu Davide anapereka zinthu zimenezi kwa Yehova pamodzi ndi siliva komanso golide wochokera ku mitundu yonse imene anagonjetsa.+ 12 Mitundu yake inali Asiriya, Amowabu,+ Aamoni, Afilisiti+ ndi Aamaleki.+ Anaperekanso zinthu zimene anatenga kwa Hadadezeri+ mwana wa Rehobu mfumu ya Zoba.

  • 2 Samueli 12:30, 31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kenako anatenga chipewa chachifumu chimene chinali kumutu kwa Malikamu* ndipo anthu anaveka Davide chipewacho. Kulemera kwake kunali kofanana ndi talente imodzi* ya golide, ndi miyala yamtengo wapatali. Iye anatenganso zinthu zambirimbiri+ mumzindawo.+ 31 Davide anatenga anthu amene anali mumzindawo nʼkuyamba kuwagwiritsa ntchito yocheka miyala, youmba njerwa komanso ntchito zina zogwiritsa ntchito zitsulo zakuthwa ndi nkhwangwa zachitsulo. Zimenezi ndi zimene anachitira anthu onse amʼmizinda ya Aamoni. Kenako Davide ndi asilikali onse anabwerera ku Yerusalemu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena