1 Mafumu 3:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Mfumu inapita ku Gibiyoni kukapereka nsembe, chifukwa kumeneko nʼkumene kunali malo okwezeka otchuka* kwambiri.+ Solomo anapereka nsembe zopsereza zokwana 1,000 paguwa lansembe.+ 1 Mbiri 16:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Zadoki+ wansembe ndi ansembe anzake anawasiya kuchihema cha Yehova chimene chinali pamalo okwezeka a ku Gibiyoni,+ 2 Mbiri 1:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Kenako Solomo ndi mpingo wonsewo anapita kumalo okwezeka ku Gibiyoni.+ Anapita kumeneko chifukwa nʼkumene kunali chihema chokumanako cha Mulungu woona, chimene Mose mtumiki wa Yehova anapanga mʼchipululu.
4 Mfumu inapita ku Gibiyoni kukapereka nsembe, chifukwa kumeneko nʼkumene kunali malo okwezeka otchuka* kwambiri.+ Solomo anapereka nsembe zopsereza zokwana 1,000 paguwa lansembe.+
39 Zadoki+ wansembe ndi ansembe anzake anawasiya kuchihema cha Yehova chimene chinali pamalo okwezeka a ku Gibiyoni,+
3 Kenako Solomo ndi mpingo wonsewo anapita kumalo okwezeka ku Gibiyoni.+ Anapita kumeneko chifukwa nʼkumene kunali chihema chokumanako cha Mulungu woona, chimene Mose mtumiki wa Yehova anapanga mʼchipululu.