Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 29:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho akalonga a nyumba za makolo, akalonga a mafuko a Aisiraeli, atsogoleri a magulu a anthu 1,000 ndi a magulu a anthu 100+ ndiponso atsogoleri oyangʼanira ntchito za mfumu,+ anabwera nʼkuyamba kupereka zinthu mwa kufuna kwawo. 7 Iwo anapereka golide wokwana matalente 5,000, madariki* 10,000, siliva wokwana matalente 10,000, kopa wokwana matalente 18,000 ndi zitsulo zokwana matalente 100,000. Anapereka zonsezi kuti zigwire ntchito panyumba ya Mulungu woona.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena