Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova, ndimakonda nyumba imene inu mumakhala,+

      Malo amene kumakhala ulemerero wanu.+

  • Salimo 27:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndapempha chinthu chimodzi kwa Yehova,

      Chimenecho ndi chimene ndikuchilakalaka.

      Chinthu chake nʼchakuti, ndikhale mʼnyumba ya Yehova masiku onse a moyo wanga,+

      Kuti ndione ubwino wa Yehova,

      Komanso kuti ndiyangʼane kachisi wake* moyamikira.*+

  • Salimo 122:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 122 Ndinasangalala pamene anandiuza kuti:

      “Tiyeni tipite kunyumba ya Yehova.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena