Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno anafuula mawu ochokera kwa Yehova otemberera guwalo, kuti: “Guwa lansembe iwe! Guwa lansembe iwe! Yehova wanena kuti, ‘Mwana wamwamuna adzabadwa mʼnyumba ya Davide, dzina lake Yosiya.+ Iye adzatenga ansembe a malo okwezeka amene akupereka nsembe yautsi pa iwe nʼkuwapereka nsembe pa iwe. Ndipo adzawotcha mafupa a anthu pa iwe.’”+

  • 2 Mafumu 23:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yosiya atatembenuka nʼkuona manda amene anali paphiri, anauza anthu kuti akatenge mafupa mʼmandawo ndipo anawatentha paguwa lansembelo. Anachititsa guwalo kukhala losayenera kulambirapo, mogwirizana ndi mawu a Yehova amene munthu wa Mulungu woona uja ananena, yemwe analosera kuti zimenezi zidzachitika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena