Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Adzadye nyamayo usiku umenewu.+ Adzaiwotche pamoto ndipo adzaidye pamodzi ndi mikate yopanda zofufumitsa+ ndi masamba owawa.+

  • Deuteronomo 16:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma muzidzapereka nsembe ya Pasikayo pamalo amene Yehova Mulungu wanu adzasankhe kuikapo dzina lake. Muzidzapereka nsembeyo madzulo, dzuwa likangolowa,+ pa nthawi yofanana ndi imene munatuluka mu Iguputo. 7 Muzidzaiwotcha nʼkuidya+ pamalo amene Yehova Mulungu wanu adzasankhe,+ ndipo mʼmawa mwake muzidzabwerera kumatenti anu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena