Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 23:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Choncho atumiki ake ananyamula mtembo wake pagaleta kuchokera ku Megido nʼkupita nawo ku Yerusalemu ndipo anakamuika mʼmanda ake. Kenako anthu amʼdzikolo anatenga Yehoahazi mwana wa Yosiya nʼkumudzoza ndiponso kumuveka ufumu mʼmalo mwa bambo ake.+

  • 2 Mbiri 34:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Nʼchifukwa chake ndidzakuika mʼmanda a makolo ako ndipo udzaikidwa mʼmanda ako mwamtendere. Maso ako sadzaona tsoka lonse lomwe ndidzabweretse pamalo ano ndi anthu ake.’”’”+

      Kenako iwo anakauza mfumuyo zimenezi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena