Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 9:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti,

      ‘Chitani zinthu mozindikira.

      Itanani akazi oimba nyimbo zoimba polira kuti abwere.+

      Ndipo tumizani anthu kuti akaitane akazi odziwa kulira maliro,

  • Yeremiya 9:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Akazi inu, tamverani mawu a Yehova.

      Tcherani khutu kuti mumve mawu otuluka mʼkamwa mwake.

      Phunzitsani ana anu aakazi kulira maliro

      Ndipo aliyense aphunzitse mnzake nyimbo yoimba polirayi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena