Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 11:1-3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ataliya,+ mayi ake a Ahaziya ataona kuti mwana wawo wafa,+ anapha anthu onse amene anali oyenera kulowa ufumu.*+ 2 Koma Yehoseba mwana wamkazi wa Mfumu Yehoramu, mchemwali wake wa Ahaziya, anaba Yehoasi+ mwana wamwamuna wa Ahaziya, pagulu la ana aamuna a mfumu amene ankayenera kuphedwa. Anatenga Yehoasi ndi mayi amene ankamusamalira nʼkukawaika mʼchipinda chamkati chogona. Anakwanitsa kubisa mwanayo kuti Ataliya asamuone, moti sanaphedwe. 3 Anakhalabe ndi mayi womusamalirayo mʼnyumba ya Yehova mmene anamubisa kwa zaka 6, pamene Ataliya ankalamulira dzikolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena