-
2 Mafumu 11:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Mʼchaka cha 7, Yehoyada anaitanitsa atsogoleri a magulu a asilikali 100 olondera mfumu a Chikariya ndiponso atsogoleri a magulu a asilikali 100 a asilikali olondera nyumba yachifumu+ ndipo anabwera kudzakumana naye kunyumba ya Yehova. Iye anachita nawo pangano nʼkuwalumbiritsa kunyumba ya Yehovayo ndipo kenako anawaonetsa mwana wa mfumu uja.+
-