Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 21:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno Abulahamu anadzuka mʼmawa kwambiri nʼkutenga mkate ndi thumba lachikopa la madzi, ndipo anaziika paphewa pa Hagara. Atatero anamuuza kuti azipita limodzi ndi mwana wakeyo.+ Choncho Hagarayo ananyamuka nʼkumangoyendayenda mʼchipululu cha Beere-seba.+

  • 2 Samueli 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 kusamutsa ufumu kuuchotsa mʼnyumba ya Sauli nʼkukhazikitsa mpando wachifumu wa Davide mu Isiraeli ndi mu Yuda, kuchokera ku Dani mpaka ku Beere-seba.”+

  • 2 Mafumu 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehoasi+ anakhala mfumu mʼchaka cha 7 cha Yehu+ ndipo analamulira ku Yerusalemu zaka 40. Mayi ake anali a ku Beere-seba+ ndipo dzina lawo linali Zibiya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena