Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 29:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pa nthawiyi, Hezekiya anaika Alevi panyumba ya Yehova atanyamula zinganga, zoimbira za zingwe ndi azeze.+ Iwo ankatsatira malamulo oimbira a Davide,+ a Gadi+ yemwe anali wamasomphenya wa mfumu, ndiponso a mneneri Natani,+ chifukwa malamulowo anachokera kwa Yehova kudzera mwa aneneri ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena