Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 9:10-13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pagulu la ansembe panali Yedaya, Yehoyaribu, Yakini+ 11 ndi Azariya mwana wa Hilikiya. Hilikiya anali mwana wa Mesulamu, Mesulamu anali mwana wa Zadoki, Zadoki anali mwana wa Merayoti ndipo Merayoti anali mwana wa Ahitubu. Ahitubu anali mtsogoleri wa nyumba* ya Mulungu woona. 12 Panalinso Adaya mwana wa Yerohamu. Yerohamu anali mwana wa Pasuri ndipo Pasuri anali mwana wa Malikiya. Komanso panali Maasai mwana wa Adieli. Adieli anali mwana wa Yahazera, Yahazera anali mwana wa Mesulamu, Mesulamu anali mwana wa Mesilemiti ndipo Mesilemiti anali mwana wa Imeri. 13 Panalinso abale awo. Onse anali atsogoleri a nyumba ya makolo awo ndipo analipo 1,760. Iwo anali amuna amphamvu ndiponso oyenerera, omwe ankatumikira panyumba ya Mulungu woona.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena