Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 8:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zimene analemba mʼmakalatawo anazipereka kuti zikhale lamulo mʼzigawo zonse. Analengeza kwa anthu a mitundu yonse nʼcholinga choti Ayuda akonzekere kudzabwezera adani awo pa tsiku limeneli.+

  • Salimo 149:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pakamwa pawo patuluke nyimbo zotamanda Mulungu,

      Ndipo lupanga lakuthwa konsekonse likhale mʼmanja mwawo,

       7 Kuti abwezere anthu a mitundu ina,

      Komanso kupereka chilango kwa mitundu ya anthu,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena